Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 3:4-6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

4. Anambadwira asanu ndi mmodzi m'Hebroni; ndi pomwepo anakhala mfumu zaka zisanu ndi ziwiri, ndi miyezi isanu ndi iwiri; ndi m'Yerusalemu anakhala mfumu zaka makumi atatu mphambu zitatu.

5. Ndipo ombadwira m'Yerusalemu ndi awa: Simeya, ndi Sobabu, ndi Natani, ndi Solomo, anai a Batisuwa mwana wamkazi wa Amieli;

6. ndi Ibara, ndi Elisama, ndi Elifeleti,

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 3