Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 24:11-26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

11. wacisanu ndi cinai Yesuwa, wakhumi Sekaniya,

12. wakhumi ndi cimodzi Eliyasibu, wakhumi ndi ciwiri Yakimu,

13. wakhumi ndi citatu Hupa, wakhumi ndi cinai Yesebeabu,

14. wakhumi ndi cisanu Biliga, wakhumi ndi cisanu ndi cimodzi Imeri,

15. wakhumi ndi cisanu ndi ciwiri Heziri, wakhumi ndi cisanu ndi citatu Hapizezi,

16. wakhumi ndi cisanu ndi cinai Petahiya, wa makumi awiri Yehezikeli,

17. wa makumi awiri ndi cimodzi Yakini, wa makumi awiri ndi ciwiri Gamuli,

18. wa makumi awiri ndi citatu Delaya, wa makumi awiri ndi cinai Miziya.

19. Awa ndi malongosoledwe ao m'utumiki wao kulowa m'nyumba ya Yehova, monga mwa ciweruzo adawapatsa Aroni atate wao, monga Yehova Mulungu wa Israyeli anamlamulira.

20. Ndipo wa ana otsala a Levi: wa ana a Amiramu, Subaeli; wa ana a Subaeli, Yedeya.

21. Wa Rehabiya: wa ana a Rehabiya, mkuru ndi Isiya.

22. Wa Aizari: Selomoti; wa ana a Selomoti, Yahati.

23. Ndi wa ana a Hebroni: mkuru ndi Yeriya, waciwiri Amariya, wacitatu Yahazieli, wacinai Yekameamu.

24. Wa ana a Uziyeli, Mika; wa ana a Mika, Samiri.

25. Mbale wa Mika, Isiya; a ana a Isiya, Zekariya,

26. Ana a Merari: Mali ndi Musi; mwana wa Yaziya, Beno.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 24