Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 24:11-17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

11. wacisanu ndi cinai Yesuwa, wakhumi Sekaniya,

12. wakhumi ndi cimodzi Eliyasibu, wakhumi ndi ciwiri Yakimu,

13. wakhumi ndi citatu Hupa, wakhumi ndi cinai Yesebeabu,

14. wakhumi ndi cisanu Biliga, wakhumi ndi cisanu ndi cimodzi Imeri,

15. wakhumi ndi cisanu ndi ciwiri Heziri, wakhumi ndi cisanu ndi citatu Hapizezi,

16. wakhumi ndi cisanu ndi cinai Petahiya, wa makumi awiri Yehezikeli,

17. wa makumi awiri ndi cimodzi Yakini, wa makumi awiri ndi ciwiri Gamuli,

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 24