Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 2:7-14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

7. Ndi ana a Karmi: Akari wobvuta Israyeliyo, amene analakwira coperekedwa ciperekereco.

8. Ndi mwana wa Etani: Azariya.

9. Ndi ana a Hezironi anambadwirawo: Yerameli, ndi Ramu, ndi Kelubai.

10. Ndi Ramu anabala Aminadabu; ndi Aminadabu anabala Nasoni kalonga wa ana a Yuda;

11. ndi Nasoni anabala Salima, ndi Salima anabala Boazi,

12. ndi Boazi anabala Obedi, ndi Obedi anabala Jese,

13. ndi Jese anabala mwana wace wamwamuna woyamba Eliabu, ndi Abinadabu waciwiri, ndi Simeya wacitatu,

14. Netaneli wacinai, Radai wacisanu,

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 2