Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 2:38-50 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

38. ndi Obedi anabala Yehu, ndi Yehu anabala Azariya,

39. ndi Azariya anabala Helezi, ndi Helezi anabala Eleasa,

40. ndi Eleasa anabala Sismai, ndi Sismai anabala Salumu,

41. ndi Salumu anabala Yekamiya, ndi Yekamiya anabala Elisama.

42. Ndi ana a Kalebi mbale wa Yerameli ndiwo Mesa mwana wace woyamba, ndiye atate wa Zifi; ndi ana a Maresa atate wa Hebroni.

43. Ndi ana a Hebroni: Kora, ndi Tapuwa, ndi Rekemu, ndi Sema.

44. Ndi Sema anabala Rahamu atate wa Yorikeamu, ndi Rekemu anabala Samai.

45. Ndi mwana wa Samai ndiye Maoni; ndipo Maoni ndiye atate wa Betizuri.

46. Ndi Efa mkazi wamng'ono wa Kalebi anabala Harani, ndi Moza, ndi Gazezi; ndi Harani anabala Gazezi.

47. Ndi ana a Yadai: Regemu, ndi Yotamu, ndi Gesam, ndi Peleti, ndi Efa, ndi Safa.

48. Maka mkazi wamng'ono wa Kalebi anabala Seberi, ndi Tirana.

49. Iyeyu anabalanso Safa atate wa Madimana, Seva atate wa Makibena, ndi atate wa Gibeya; ndi mwana wamkazi wa Kalebi ndiye Akisa.

50. Ana a Kalebi ndi awa: mwana wa Huri, mwana woyamba wa Efrata, Sobali atate wa Kiriate Yearimu.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 2