Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 2:34-45 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

34. Ndipo Sesani analibe ana amuna, koma ana akazi. Ndi Sesani anali naye mnyamata M-aigupto dzina lace ndiye Yara.

35. Ndipo Sesani anampatsa Yara mnyamata wace mwana wace wamkazi akhale mkazi wace, ndipo anambalira Atai.

36. Ndipo Atai anabala Natani, ndi Natani anabala Zabadi,

37. ndi Zabadi anabala Efilali, ndi Efilali anabala Obedi,

38. ndi Obedi anabala Yehu, ndi Yehu anabala Azariya,

39. ndi Azariya anabala Helezi, ndi Helezi anabala Eleasa,

40. ndi Eleasa anabala Sismai, ndi Sismai anabala Salumu,

41. ndi Salumu anabala Yekamiya, ndi Yekamiya anabala Elisama.

42. Ndi ana a Kalebi mbale wa Yerameli ndiwo Mesa mwana wace woyamba, ndiye atate wa Zifi; ndi ana a Maresa atate wa Hebroni.

43. Ndi ana a Hebroni: Kora, ndi Tapuwa, ndi Rekemu, ndi Sema.

44. Ndi Sema anabala Rahamu atate wa Yorikeamu, ndi Rekemu anabala Samai.

45. Ndi mwana wa Samai ndiye Maoni; ndipo Maoni ndiye atate wa Betizuri.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 2