Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 2:14-18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

14. Netaneli wacinai, Radai wacisanu,

15. Ozemu wacisanu ndi cimodzi, Davide wacisanu ndi ciwiri;

16. ndi alongo ao ndiwo Zeruya ndi Abigaili. Ndi ana a Zeruya: Abisai ndi Yoabu, ndi Asaheli; atatu.

17. Ndi Abigaili anabala Amasa; ndi atate wa Amasa ndiye Yeteri M-ismayeli.

18. Ndi Kalebi mwana wa Hezroni anabala ana ndi Azuba mkazi wace, ndi Yerioti; ndipo ana ace ndiwo Yeseri, ndi Sobabu, ndi Aridoni.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 2