Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 2:13-19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

13. ndi Jese anabala mwana wace wamwamuna woyamba Eliabu, ndi Abinadabu waciwiri, ndi Simeya wacitatu,

14. Netaneli wacinai, Radai wacisanu,

15. Ozemu wacisanu ndi cimodzi, Davide wacisanu ndi ciwiri;

16. ndi alongo ao ndiwo Zeruya ndi Abigaili. Ndi ana a Zeruya: Abisai ndi Yoabu, ndi Asaheli; atatu.

17. Ndi Abigaili anabala Amasa; ndi atate wa Amasa ndiye Yeteri M-ismayeli.

18. Ndi Kalebi mwana wa Hezroni anabala ana ndi Azuba mkazi wace, ndi Yerioti; ndipo ana ace ndiwo Yeseri, ndi Sobabu, ndi Aridoni.

19. Namwalira Azuba, ndi Kalebi anadzitengera Efrati, amene anambalira Huri.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 2