Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 19:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene ana a Amoni anaona kuti anadzinunkhitsa kwa Davide, Hanuni ndi ana a Amoni anatumiza matalente cikwi cimodzi a siliva, kudzilembera magareta ndi apakavalo ku Mesopotamiya, ndi ku Aramu-maaka, ndi ku Zoba.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 19

Onani 1 Mbiri 19:6 nkhani