Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 18:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Aaramu a ku Damasiko anadza kudzathandiza Hadarezeri mfumu ya Zoba; koma Davide anakantha Aaramu amuna zikwi makumi awiri mphambu ziwiri.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 18

Onani 1 Mbiri 18:5 nkhani