Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 18:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Izi zomwe mfumu Davide anazipatulira Yehova, pamodzi ndi siliva ndi golidi adazitenga kwa amitundu onse, kwa Edomu, ndi kwa Moabu, ndi kwa ana a Amoni, ndi kwa Afilisti, ndi kwa Amaleki.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 18

Onani 1 Mbiri 18:11 nkhani