Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 15:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti, cifukwa ca kusalinyamula inu poyamba paja, Yehova Mulungu wathu anacita cotipasula, popeza sitinamfunafuma Iye monga mwa ciweruzo.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 15

Onani 1 Mbiri 15:13 nkhani