Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 14:4-8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

4. Maina a ana anali nao m'Yerusalemu ndi awa: Samna, ndi Sobabu Natani, ndi Solomo,

5. ndi Ibara, ndi Elisua, ndi Elipeleti,

6. ndi Noga, ndi Nefegi, ndi Yafiya,

7. ndi Elisama, ndi Beliyada, ndi Elifeleti.

8. Pamene Afilisti anamva kuti anamdzoza Davide akhale mfumu ya Aisrayeli onse, Afilisti onse anakwera kufunafuna Davide; ndipo Davide anamva, nawaturukira.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 14