Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 12:5-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

5. Eluzai, ndi Yerimoti, ndi Bealiya, ndi Semariya, ndi Sefatiya wa ku Harupi,

6. Elikana, ndi Isiya, ndi Azereli, ndi Yoezeri, ndi Yasobeamu ndiwo Akora;

7. ndi Yoda, ndi Zebadiya, ana a Yerohamu wa ku Gedoro.

8. Ndi Agadi ena anapambukira kwa Davide ku liogala m'cipululu, ngwazi zamphamvu zozerewera nkhondo, zogwira cikopa ndi mkondo; nkhope zao zikunga nkhope za mikango, ndi liwiro lao longa la ngoma kumapiri:

9. Ezeri mkuru wao, waciwiri Obadiya, wacitatu Eliabu,

10. wacinai Misimana, wacisanu Yeremiya,

11. wacisanu ndi cimodzi Atai, wacisanu ndi ciwiri Elieli,

12. wacisanu ndi citatu Yohanani, wacisanu ndi cinai Elzabadi,

13. wakhumi Yeremiya, wakhumi ndi cimodzi Makibanai.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 12