Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 1:43 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mafumu tsono akucita ufumu m'dziko la Edomu, pakalibe mfumu wakucita ufumu pa ana a Israyeli, ndiwo Bela mwana wa Beori; ndi dzina la mudzi wace ndilo Dinaba.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 1

Onani 1 Mbiri 1:43 nkhani