Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 1:3-14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Enoki, Metusela, Lameki,

4. Nowa, Semu, Hamu, ndi Yafeti.

5. Ana a Yafeti: Gomeri, ndi Magogi, ndi Madai, ndi Yavani, ndi Tubala, ndi Meseki, ndi Tirasi.

6. Ndi ana a Gomeri: Asikenazi, Difati, ndi Togarima.

7. Ndi ana a Yavani: Elisa, ndi Tarisisa, Kitimu, ndi Rodanimu.

8. Ana a Hamu: Kusi, ndi Mizraimu, Puti, ndi Kanani.

9. Ndi ana a Kusi: Seba, ndi Havila, ndi Sabita, ndi Rama, ndi Sabteka. Ndi ana a Rama: Seba, ndi Dedani.

10. Ndi Kusi anabala Nimmdi; iye anayamba kukhala wamphamvu pa dziko.

11. Ndi Mizraimu anabala Aludi, ndi Aanami, ndi Alehabi, ndi Anaftuki,

12. ndi Apatrusi, ndi Akasluki, (kumene anafuma Afilisti), ndi Akafitori.

13. Ndi Kanani anabala Zidoni mwana wace woyamba, ndi Heti,

14. ndi Ayebusi, ndi Aamori, ndi Agirigasi,

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 1