Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 1:18-36 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

18. Ndi Aripakisadi anabala Sela; ndi Sela anabala Eberi.

19. Ndi Eberi anabala ana amuna awiri, dzina la winayo ndiye Pelegi, popeza masiku ace dziko linagawanika; ndi dzina la mbale wace ndiye Yokitani.

20. Ndipo Yokitani anabala Almodadi, ndi Selefi, ndi Hazaramaveti, ndi Yera;

21. ndi Hadoramu, ndi Uzali, ndi Dikila;

22. ndi Ebala, ndi Abimaele, ndi Seba,

23. ndi Ofiri, ndi Havila, ndi Yobabi. Awa onse ndiwo ana a Yokitani.

24. Semu, Aripakisadi, Sela;

25. Eberi, Pelegi, Reu,

26. Serugi, Nahori, Tera;

27. Abramu, (ndiye Abrahamu).

28. Ana a Abrahamu: Isake, ndi Ismayeli.

29. Mibadwo yao ndi awa; woyamba wa Ismayeli Nebayoti; ndi Kedara ndi Adibeli, ndi Mibisamu,

30. Misma, ndi Duma Masa,

31. Hadada, ndi Tema, Nafisi, ndi Kedema. Awa ndi ana a Ismayeli.

32. Ndi ana a Ketura mkazi wamng'ono wa Abrahamu anabala Zimiramu, ndi Yokisani, ndi Medani, ndi Midyani, ndi Isibaki, ndi Sua. Ndi ana a Yokisani: Seba, ndi Dedani.

33. Ndi ana a Midyani: Efa, ndi Eferi, ndi Hanoki, ndi Abida, ndi Elidaa. Awa onse ndiwo ana a Ketura.

34. Ndipo Abrahamu anabala Isake. Ana a Isake: Esau, ndi Israyeli.

35. Ana a Esau: Elifazi, Reueli, ndi Yeuzi, ndi Yolamu, ndi Kora.

36. Ana a Elifazi: Teani, ndi Omara, Zefi, ndi Gatamu, Kenazi, ndi Timna, ndi Amaleki.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 1