Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 9:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndi midzi yonse yosungamo zinthu zace za Solomo, ndi midzi yosungamo magareta ace, ndi midzi yokhalamo apakavalo ace, ndi zina ziti zonse zidakomera Solomo kuzimanga m'Yerusalemu, ndi ku Lebano, ndi m'dziko lonse la ufumu wace.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 9

Onani 1 Mafumu 9:19 nkhani