Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 8:53 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Popeza Inu munawapatula pa anthu onse a pa dziko lapansi akhale colowa canu, monga munanena ndi dzanja la Mose mtumiki wanu, pamene munaturutsa makolo athu m'Aigupto, Yehova Mulungu Inu.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 8

Onani 1 Mafumu 8:53 nkhani