Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 8:36 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

pamenepo mverani Inu m'Mwamba, ndi kukhululukira cimo la akapolo anu, ndi la, anthu anu Aisrayeli; pakuti muwaphunzitsa njira yokoma ayenera kuyendamo, ndi kupatsa mvula pa: dziko lanu, limene munawapatsa anthu anu likhale colowa cao.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 8

Onani 1 Mafumu 8:36 nkhani