Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 6:32 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Zitseko ziwiri zomwe zinali za mtengo waazitona, anasemapo ngati akerubi ndi migwalangwa ndi maluwa oti gada, nawakuta ndi golidi; inde anakutanso ndi golidi akerubi ndi migwalangwayo.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 6

Onani 1 Mafumu 6:32 nkhani