Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 4:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Solomo anali nao akapitao khumi ndi awiri akuyang'anira Aisrayeli onse, akufikitsira mfumu ndi banja lace zakudya; ali yense anafikitsa zakudya zofikira mwezi umodzi wa caka.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 4

Onani 1 Mafumu 4:7 nkhani