Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 4:1-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo mfumu Solomo anali mfumu ya Israyeli yense.

2. Ndipo akuru a mfumu ndi awa: Azariya mwana wa Zadoki anali nduna,

3. Elihorepa ndi Ahiya ana a Sisa alembi, Yehosafati mwana wa Ahiludi wolembera mbiri,

4. ndi Benaya mwana wa Yehoyada anali kazembe wa nkhondo, ndi Zadoki ndi Abyatara anali ansembe,

5. ndi Azariya mwana wa Natani anayang'anira akapitao, ndi Zabudi mwana wa Natani anali nduna yopangira mfumu,

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 4