Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 22:34 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo munthu anakoka uta wace ciponyeponye, nalasa mfumu ya Israyeli pakati pa maluma a maraya acitsulo; tsono ananena ndi mnyamata wa gareta wace, Tembenuza dzanja lako, nundicotse kunkhondo, popeza ndalasidwa.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 22

Onani 1 Mafumu 22:34 nkhani