Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 22:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo atafika kwa mfumu, mfumu inati kwa iye, Mikaya, kodi tizimuka ku Ramoti Gileadi kukathira nkhondo, kapena tileke? Nati iye, Kwerani, ndipo mudzacita mwai, popeza Yehova adzaupereka m'dzanja la mfumu.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 22

Onani 1 Mafumu 22:15 nkhani