Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 21:29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Waona umo wadzicepetsera Ahabu pamaso panga? Popeza adzicepetsa pamaso panga, sindidzafikitsa coipa cimeneci akali moyo iye; koma m'masiku a mwana wace ndidzacifikitsa pa nyumba yace.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 21

Onani 1 Mafumu 21:29 nkhani