Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 21:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anthu aja awiri oipawo analowa, nakhala pamaso pace, ndipo anthu oipawo anamcitira umboni wonama Nabotiyo, pamaso pa anthu onse, nati, Naboti anatemberera Mulungu ndi mfumu. Pamenepo anamturutsa m'mudzi, namponya miyala, namupha.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 21

Onani 1 Mafumu 21:13 nkhani