Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 20:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ali yense anapha munthu wace; ndipo Aaramu anathawa, Aisrayeli nawapitikitsa; ndipo Benihadadi mfumu ya Aramu anathawira pa kavalo pamodzi ndi apakavalo.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 20

Onani 1 Mafumu 20:20 nkhani