Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 2:39 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunacitika, zitapita zaka zitatu, kuti akapolo awiri a Simeyi anathawira kwa Akisi mwana wa Maaka mfumu ya Gati. Ndipo anamuuza Simeyi, nati, Taonani, akapolo anu akhala ku Gati.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 2

Onani 1 Mafumu 2:39 nkhani