Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 2:30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nafika Benaya ku cihema ca Yehova, nati kwa iye, Mfumu itero, Taturuka. Nati, Iai, koma ndifere pompano. Ndipo Benaya anabweza mau kwa mfumu, nati, Yoabu wanena cakuti, nandiyankha mwakuti mwakuti.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 2

Onani 1 Mafumu 2:30 nkhani