Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 2:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mfumu inanena ndi Abyatara wansembeyo, Pita ku Anatoti ku minda yako; pakuti wakutidwa ndi imfa; koma sindikupha iwe lero lino, cifukwa unanyamula likasa la Ambuye Yehova pamaso pa Davide atate wanga, ndi popeza unazunzidwa monse umo atate wanga Davide anazunzidwamo.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 2

Onani 1 Mafumu 2:26 nkhani