Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 2:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo masiku ace akukhala Davide mfumu ya Israyeli anali zaka makumi anai; zaka zisanu ndi ziwiri anakhala mfumu ku Hebroni, ndi zaka makumi atatu mphambu citatu anakhala mfumu ku Yerusalemu.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 2

Onani 1 Mafumu 2:11 nkhani