Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 19:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anabwerera panali iye uja, natengako ng'ombe ziwiri, nazipha, naphikira nyama yace ndi zipangizo za zocitira nazo ng'ombe, napatsa anthu adye. Atatero, ananyamuka, natsata Eliya, namtumikira.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 19

Onani 1 Mafumu 19:21 nkhani