Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 19:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tsono Yezebeli anatuma mthenga kwa Eliya, wakuti, Milungu indilange nionjezepo, ngati sindilinganiza moyo wako ndi moyo wa mmodzi wa iwowo mawa nthawi yomwe yino.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 19

Onani 1 Mafumu 19:2 nkhani