Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 19:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tsono anacokako, napeza Elisa mwana wa Safati alikukoketsa cikhasu ng'ombe ziwiri ziwiri magori khumi ndi awiri, iye yekha anakhala pa gori lakhumi ndi ciwiri; ndipo Eliya anamka kunali iyeyo, naponya copfunda cace pa iye.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 19

Onani 1 Mafumu 19:19 nkhani