Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 18:37 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndimvereni Yehova, ndimvereni, kuti anthu awa adziwe kuti Inu Yehova ndinu Mulungu, ndi kuti Inu mwabwezanso mitima yao.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 18

Onani 1 Mafumu 18:37 nkhani