Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 18:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo atapita masiku ambiri, mau a Yehova anafika kwa Eliya caka cacitatu, nati, Kadzionetse kwa Ahabu, ndipo ndidzatumiza mvula padziko.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 18

Onani 1 Mafumu 18:1 nkhani