Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 16:31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali monga ngati kunamcepera kuyenda m'macimo a Yerobiamu mwana wa Nebati, iye anakwatira Yezebeli mwana wamkazi wa Etibaala mfumu ya Azidoni, natumikira Baala, namgwadira,

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 16

Onani 1 Mafumu 16:31 nkhani