Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 15:33 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tsono Basa mwana wa Ahiya analowa ufumu wa Israyeli caka cacitatu ca Asa mfumu ya Yuda, nakhala mfumu ku Tiriza zaka makomi awiri mphambu zinai.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 15

Onani 1 Mafumu 15:33 nkhani