Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 15:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tsono Asa anatenga siliva yense ndi golidi yense anatsala pa cuma ca nyumba ya Yehova, ndi cuma ciri m'nyumba ya mfumu, nazipereka m'manja mwa anyamata ace; ndipo mfumu Asa anazitumiza kwa Benihadadi mwana wa Tabrimoni, mwana wa Hezroni mfumu ya Aramu, wakukhala ku Damasiko, nati,

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 15

Onani 1 Mafumu 15:18 nkhani