Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 14:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Natero mkazi wa Yerobiamu, nanyamuka namka ku Silo, nalowa m'nyumba ya Ahiya. Koma Ahiya sanatha kupenya, popeza maso ace anali tong'o, cifukwa ca ukalamba wace.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 14

Onani 1 Mafumu 14:4 nkhani