Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 13:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo munthu wa Mulungu ananena ndi mfumu, Mungakhale mundigawira pakati ndi pakati nyumba yanu, sindilowa kwa inu, kapena kudya mkate, kapena kumwa madzi kuno.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 13

Onani 1 Mafumu 13:8 nkhani