Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 12:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Anthu awa akamakwera kukapereka nsembe m'nyumba ya Yehova m'Yerusalemu, pamenepo mitima ya anthu awa idzatembenukiranso kwa mbuye wao, kwa Rehabiamu mfumu ya Yuda; ndipo adzandipha, nadzabweranso kwa Rehabiamu mfumu ya Yuda.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 12

Onani 1 Mafumu 12:27 nkhani