Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 12:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Rehabiamu anafika ku Yerusalemu, nasonkhanitsa nyumba yonse ya Yuda, ndi pfuko la Benjamini, ankhondo osankhika zikwi zana limodzi mphambu makumi asanu ndi atatu, kuyambana nayo nyumba ya Israyeli, kubwezanso ufumu kwa Rehabiamu mwana wa Solomo.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 12

Onani 1 Mafumu 12:21 nkhani