Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 11:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mfumu Solomo anakonda akazi ambiri acilendo, pamodzi ndi mwana wamkazi wa Farao, akazi a ku Moabu, ndi a ku Amoni, ndi a ku Edomu, ndi a ku Zidoni, ndi Ahiti;

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 11

Onani 1 Mafumu 11:1 nkhani