Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 10:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mpandowo wacifumu unali ndi makwerero asanu ndi limodzi, ndi pamwamba pa mpando wacifumu panali pozungulira kumbuyoko, ndipo munali ngati manja m'mbali zonse ziwiri za pokhalirapo, naimika mikango iwiri m'mbali mwa manjawo.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 10

Onani 1 Mafumu 10:19 nkhani