40. Ndipo anakhala pansi mabungwe mabungwe a makumi khumi, ndi a makumi asanu.
41. Ndipo Iye anatenga mikate isanuyo ndi nsomba ziwirizo nayang'anakumwamba, nadalitsa, nagawa mikate; napatsa kwa ophunzira kuti apereke kwa iwo; ndi nsomba ziwiri anagawira onsewo.
42. Ndipo anadya iwo onse, nakhuta.
43. Ndipo anatola makombo mitanga khumi ndi iwiri, ndiponso za nsomba.