50. Ndipo anaturuka nao kufikira ku Betaniya; nakweza manja ace, nawadalitsa.
51. Ndipo kunali, 13 pakuwadalitsa iye analekana nao, natengedwa kunka Kumwamba.
52. Ndipo 14 anamlambira iye, nabwera ku Yerusalemu ndi cimwemwe cacikuru;
53. ndipo IS anakhala ci khalire m'Kacisi, nalikuyamika Mulungu, Amen.