2. Yehova akonda zipata za ZiyoniKoposa zokhalamo zonse za Yakobo.
3. Mudzi wa Mulungu, inu,Akunenerani zakukulemekezani.
4. Ndidzachula Rahabu ndi Babulo kwa iwo ondidziwa Ine;Taonani, Filistiya ndi Turo pamodzi ndi Kusi;Uyu anabadwa komweko.
5. Ndipo adzanena za Ziyoni,Uyu ndi uyo anabadwa m'mwemo;Ndipo Wam'mwambamwamba ndiye aclzaukhazikitsa.
6. Yehova adzawerenga, polembera mitundu ya anthu.Uyu anabadwa komweko.
7. Ndipo oyimba ndi oomba omwe adzati,Akasupe ansa onse ali mwa inu.