10. Mphamvu ya kavalo siimkonda:Sakondwera nayo miyendo ya munthu.
11. Yehova akondwera nao akumuopa Iye,Iwo akuyembekeza cifundo cace.
12. Yerusalemu, lemekezani Yehova;Ziyoni, lemekezani Mulungu wanu.
13. Popeza analimbitsa mipiringidzo ya zitseko zanu:Anadalitsa ana anu m'kati mwanu.